Chifukwa Chenicheni Chomwe Shepherd Bushiri Akumangira Mzinda Wa GOSHEN CITY

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 11 ก.ย. 2024
  • if you like my content and would like to support me further, please
    PayPal
    ➡️To Donate please use PayPal www.paypal.me/...
    Business/Sponsor Inquiries //hanifamw.suggestions@gmail.com
    Mu November mchaka cha 2021, pamene mlaliki Shepherd Bushiri pamodzi ndi mkazi wake Mary anathawa belo mdziko la South Africa mkubwera kuno ku Malawi, anthu ambiri anayesa kuti basi watha ndipo sangapangenso chilichonse cholozeka. Hotel yake yotchedwa Sparkling and Spa yomwe ili mu dera wa Rustenburg mdzikolo inayamba kupita pansi popeza malonda sankayenda. Ndalama zomwe amkazipeza kuchoka mu chopereka chaku tchalichi kamba kakuthawaku izi zinayima. Kenako ali ku Malawi analengeza za scholarship yomwe iye akufuna kuthandiza ana osowa fees mma sukulu osiyanasiyana. Apa anthu sanamukhulupilire popeza amkati alibe ndalama ndipo amapanga izi pongofuna kutchuka.
    Komatu Bushiri wadabwitsa ndikututumutsa anthu ambiri posachedwapa atalengeza kuti akumanga mzinda m’boma wa Mangochi womwe akuwutcha kuti Goshen City.

ความคิดเห็น • 124

  • @LovenessLester
    @LovenessLester 2 หลายเดือนก่อน +1

    That's a great city for many Malawians let's learn how to appreciate this our man of God 🙏

  • @alfednjolobvi1591
    @alfednjolobvi1591 2 ปีที่แล้ว +5

    Bushiri ur a great man that's why ur very blessed I wish if Malawi having too many people like u Bushiri who thinking about there homeland ur great indeed keep it up God bless you more

  • @michealmwimba6084
    @michealmwimba6084 ปีที่แล้ว +3

    I just like the way you express yourself in chichewa its so amazing and keep up the good work

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe7231 2 ปีที่แล้ว +5

    I salute Bushiri, he is one of a kind
    Creating jobs for the young people

  • @josephkaputa8502
    @josephkaputa8502 2 ปีที่แล้ว +3

    He is agood man coz he is dealing with poverty,big up B

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 2 ปีที่แล้ว +17

    He is doing great work to develop Malawi

  • @lucksonlongwe1658
    @lucksonlongwe1658 2 ปีที่แล้ว +4

    Best wishes to man of God. Continue your work. God is with you.

  • @joebanda3732
    @joebanda3732 2 ปีที่แล้ว +3

    You are doing extremely well Sir I like your tone. U got a very bright future. God will exalt you this year. Stay focused and pray more

  • @teddybanda8989
    @teddybanda8989 2 ปีที่แล้ว +12

    That guy has got gold mines here in zambia 🇿🇲 and different countries

  • @mollymadzibane
    @mollymadzibane ปีที่แล้ว

    My Father My Prophet you are doing great job . You are creating work also for Malawians generation . I tap into your Annointing my Prophet . May God bless you all your Enemies will Scarter one by one Molly limpopo

  • @madakasosoch4322
    @madakasosoch4322 ปีที่แล้ว +3

    He is going great work to develop Malawi

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 ปีที่แล้ว +2

    Hard workers always think about changing things .All the best man

  • @isaacschamatwa3596
    @isaacschamatwa3596 2 ปีที่แล้ว +1

    such a very good tone,Bushiri is doing such a good job

  • @williamlahman2787
    @williamlahman2787 2 ปีที่แล้ว +1

    Let him to fulfill his duties,. He's so young, hope will do mo than that. All those jealous people must fall. Almighty bless him

  • @stevechizaka9908
    @stevechizaka9908 2 ปีที่แล้ว +3

    Dziko la malawi silimatukuka ndi nkhani ngati zimenezi. Munthu ngati akumanga town yamakono ngati imeneyi mudziko lathu.ife bwezi tikuonesa chikondi kwaiye ndikumulimbikisa osati kumufookesa pazinkhani zopanda Pache. Anthu akatangale akuwaziwa kale bwanji osamakawafufuza amenewo

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 ปีที่แล้ว +2

    Goshen City is a product of powerful vision

  • @biggyk7740
    @biggyk7740 2 ปีที่แล้ว

    I will always support bushiri he is a true citizen of Malawi

  • @harrietmwika8695
    @harrietmwika8695 ปีที่แล้ว +1

    Love the Bushiris keep it up and God bless.

  • @mussawilliam5684
    @mussawilliam5684 2 ปีที่แล้ว +2

    Vuto ndilokuti ife a malawi makamaka kumipandoko kwachuluka achule kwambili mwachisanzo ine ndili kuno ku south Africa ndapedza ndalama ndithawile dziko lakwathu adzafuna kundifufudza ndiye uchulewo ugalu a aphaka Bushili akufuna kutukula dziko lakumalawi ndiye pakupedzeka agalu ena monga amulaka malilo ndijelasi yao kudzolowela kuvutika ugalu basi Bushiri akufuna kutukula dziko lamalawi

  • @hoekboy1102
    @hoekboy1102 2 ปีที่แล้ว +3

    I salute you Bushiri I will be Uber driver there

  • @maxwellmustaffaalickalick1745
    @maxwellmustaffaalickalick1745 2 ปีที่แล้ว +1

    Ife anthu akuda ndichoncho sanje kwambiri i respect him a lot

  • @mederinausain6913
    @mederinausain6913 ปีที่แล้ว +1

    Bushili ndi one akupotsa president ulemu wanu a bushili za ndare simupanga nawo koma kukwedza malawi pa sogolo ..koma muzandilembeko tchito

  • @machonabanda5752
    @machonabanda5752 2 ปีที่แล้ว +5

    Hanifa you are the best ♥️♥️🙏🙏

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 ปีที่แล้ว +2

    Good work Prophet Bushiri

  • @benitozack6523
    @benitozack6523 ปีที่แล้ว

    Don't be jealous with someone who is doing great work,because that city will change many Malawians

  • @englishboy6570
    @englishboy6570 2 ปีที่แล้ว +4

    Vuto la amalawi ndinsanje basi

    • @jestinanamkonda1495
      @jestinanamkonda1495 2 ปีที่แล้ว +2

      That is the problem of Malawians

    • @jtpi8362
      @jtpi8362 2 ปีที่แล้ว +1

      Ndi izi mukuziona ku ma comments kuno, anthu a nsanje akumunyozabe m'malo moyamikila kuti a Malawi ambiri apeza ntchito kumeneko, komanso dziko lathu litchuka ntchito imeneyi ikatha.

  • @agnessmpungalume1446
    @agnessmpungalume1446 ปีที่แล้ว

    Just wow
    Beautiful masophenya

  • @jestinanamkonda1495
    @jestinanamkonda1495 2 ปีที่แล้ว +4

    The annointing of Papa Bushiri breaks the yokes of poverty. Try it. You don't know the businesses Bushiri has. Why being so rough without the knowledge of his wealth and Riches. He is the third richest person in Malawi nde mumati ndalama azitani nazo?
    They devil will never be happy with a progressive person

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe7231 2 ปีที่แล้ว +6

    Please do the same content in English to enable none Malawians understand
    Unless you are from Zambia and some Zimbabwians can understand

    • @brucewarchild2156
      @brucewarchild2156 2 ปีที่แล้ว

      It's none of foreigners business

    • @chifundonkhoma3642
      @chifundonkhoma3642 2 ปีที่แล้ว

      Kkkkkkk OK fine.... Please people stop being jealous,instead of focusing on your demonic poverty , you waste time with whom YAHWE blessed... Learn to love one another.. Learn to thank God......

  • @willardakidy6916
    @willardakidy6916 2 ปีที่แล้ว +1

    Akulephera mapulesident kutukura dziko lanthu ineyo ndingoti Malawi mwana tingathe kumaloza chala kwaathu kuti town yakwathu iyo mulungu pasongolo basi

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 ปีที่แล้ว

    We need ro underatand in english too. Inam in South Africa.

  • @Fanny-h9r
    @Fanny-h9r 19 วันที่ผ่านมา

    Boozaa anthu ake ati omwe alembedwa ntchitowo mphekesela ya boza iyii

  • @trymoo8479
    @trymoo8479 2 ปีที่แล้ว +2

    Ohhh? At least

  • @limpopolimpopo2623
    @limpopolimpopo2623 2 ปีที่แล้ว +2

    A Malawi sanje mlekeni atukule dziko lathu la Malawi

  • @gloriabanda6552
    @gloriabanda6552 2 ปีที่แล้ว +1

    this is great💯

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 2 หลายเดือนก่อน

    Akurephera chakwera kutukura ziko.rino angoononga ndarama chakwera chito zamanja ako zikuchitire umboni bushiri

  • @wisdomktitus660
    @wisdomktitus660 ปีที่แล้ว

    Aaa pajatu Malawi is full of kaduka,,enawa angofuna amudyere

  • @ThomasMwandila-tn7cf
    @ThomasMwandila-tn7cf 21 วันที่ผ่านมา

    Murekeni munthu atukure marawi

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 ปีที่แล้ว

    Man of God who only does God mind not him

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q 2 หลายเดือนก่อน

    Bushiri uzangokhara president

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 2 ปีที่แล้ว +3

    A Malawi Munatani kodi kumangovuta pa zinthu zopanda pake MAJOR 1 akufuna kutimagira Town mukufuna kumufufuza chiyani at least he's creating jobs zomwe Atsogoleri athu saangakwanitse koma kuba basi ndi ma slangs and fluent English opanda pake hands of BUSHIRI Manga Town SHEPHERD...👏👏💪 Let Them Talk, Idiot's come on Homies If you want someone to investigate I'm gonna show you where to go Pitani ku TONSE ALLIANCE that's where you'll find thieves,mbava,akamatule,matsotsi,wawii,🤞😊

  • @mbumbajilowele6511
    @mbumbajilowele6511 2 ปีที่แล้ว

    Greatest man

  • @anthuochukapazambiaelishas4978
    @anthuochukapazambiaelishas4978 2 ปีที่แล้ว +1

    Perfect

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma3642 2 ปีที่แล้ว +1

    Komatu anthu mupole moto... Mmalo mopanga njira zothana ndi umphawi omwe satana anakutembererani nawowo.. Mukulimbana ndiwo mulungu adawadalitsa, kutaya nthawi ndi za zii limbikirani kupemphera siyani msanje, mulungu adzaona mokudalitsira musiyeni Shepherd Bushiri apange zothandiza human kind

  • @bashiriyusufu1224
    @bashiriyusufu1224 2 ปีที่แล้ว

    🔥🔥🔥Wabwela ngat coming
    💪💪💪

  • @williamjusten6646
    @williamjusten6646 2 ปีที่แล้ว +1

    Great job

  • @mikegoodblessyoumenofgoodm3482
    @mikegoodblessyoumenofgoodm3482 2 ปีที่แล้ว +1

    Moti musangalale akubwelesa
    Chitukuko ku malawi sanjebasi

  • @johnboscozgambo71
    @johnboscozgambo71 2 ปีที่แล้ว

    Thanks for budget

  • @promise3693
    @promise3693 2 ปีที่แล้ว +1

    Nsanje aMalawi iiiii munthu akapanga chinthu basi zokamba mbweeee

  • @innocentkandulu2825
    @innocentkandulu2825 2 ปีที่แล้ว

    That's great

  • @praisemkutumula3348
    @praisemkutumula3348 ปีที่แล้ว

    Great ideas

  • @thomphalavi5027
    @thomphalavi5027 21 วันที่ผ่านมา

    Mzinda umeneu u kubwera ndizolinga chilipo akufuna ku Malawi kuno ndpo zomwe anthu awa zolinga zawo zikwanilitsidwa ndipo akufuna Malawi ankhale mbali imodz yaa tow omwe amachita za satana

  • @AllanChingwazala
    @AllanChingwazala 2 หลายเดือนก่อน

    Ndimafunisisa utazakhara president malawi ikhoza kukhala yopambana ngat wakwanisa kumanga ndalama zayekha kulibwanji athakhala president buchiri ndimakufila kuzakhala president ndizabwerera kumalawi

  • @beautyandnatureofafrica5334
    @beautyandnatureofafrica5334 2 ปีที่แล้ว

    Nsanje amalawi.. Musiyen bushiri atukule dzulo lathu

  • @geoffreychimutu6654
    @geoffreychimutu6654 ปีที่แล้ว

    More fire

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 2 ปีที่แล้ว +1

    Gays tangoyamikilani muthuyu popangachiganizo chotukula zikolovesa chisonili ngati palizolakwika aakoze ndimulungu

    • @olipamaseko2693
      @olipamaseko2693 10 หลายเดือนก่อน

      Zokaikitsa ndalama zake aaa

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 9 หลายเดือนก่อน

      @@olipamaseko2693and so???? Nde mukufuna kuti munthu atani kodi. Olo Chakwera atasiya kupusa kwakeku this country can’t still go further because of people like you. Bitter and pathetic person

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 ปีที่แล้ว

    I like profet he only does God mind not his

  • @webbyasterchengo4006
    @webbyasterchengo4006 2 ปีที่แล้ว +1

    That's why ziko lamalawi lizakalabe losauka mphaka kale kale amufufuza bwanji ngati ziko lamalawi labeledwapo nsaja basi ziko losafuninara anthu zabwino

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 9 หลายเดือนก่อน

      Ndipo iyi nde ndi mfundo ndithu

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 2 ปีที่แล้ว +2

    Ppl are serious wth him ......for show bushiri is doing good jobs for better malawians

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 7 หลายเดือนก่อน

    Zoona zake afufuzidwee munali asadiki miya muzikomo olemera oti amatha kukuthandiza boma lo koma sanafikepo apo fufuzani ndithu

  • @phikamomo9755
    @phikamomo9755 ปีที่แล้ว

    Nice job

  • @thekuhespodcast
    @thekuhespodcast 2 ปีที่แล้ว +1

    The first to comment and hopefully will be the first resident of Goshen 😂

  • @newdavidomw
    @newdavidomw ปีที่แล้ว

    bushiri ndi munthu modzi wachuma yemwe akuyika pa map malawi

  • @nelsonkausiwa4754
    @nelsonkausiwa4754 ปีที่แล้ว

    Major one

  • @bonimpoya1439
    @bonimpoya1439 ปีที่แล้ว

    Malawi goas on

  • @giftphiri595
    @giftphiri595 2 ปีที่แล้ว

    A Malawi ambiri amadana ndi chitukuko amafuna kuba chabe, Bushiri asaope munthu.

  • @hendmorsoni32
    @hendmorsoni32 ปีที่แล้ว

    Malawi akukanika kutukuka chifukwa chansanje

  • @johnbihali9883
    @johnbihali9883 ปีที่แล้ว

    But your report doesn't relate with the title of your presentation. Improve pliz

  • @kondwanileonard9868
    @kondwanileonard9868 2 ปีที่แล้ว

    Is right

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos1484 2 ปีที่แล้ว

    Humm

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 ปีที่แล้ว

    Maiko azathu anthu ngati amene ndi amene amatukura dziko,

  • @manuelsamuel293
    @manuelsamuel293 2 ปีที่แล้ว +1

    Let him to do what he want to do and moreover he is doing that in his country, so let those dogs who has jealous with him to smile urine

  • @cadohjabu5565
    @cadohjabu5565 2 ปีที่แล้ว +1

    Mlandu Ukudikila ku South Africa Aonetse chitsanzo chabwino

  • @mabvutochimkondenji910
    @mabvutochimkondenji910 2 หลายเดือนก่อน

    uyu akhale vice

  • @innocentchirwa3677
    @innocentchirwa3677 2 ปีที่แล้ว

    Wabwera mwa coming

  • @snetawailiyasa3215
    @snetawailiyasa3215 2 ปีที่แล้ว

    Ok

  • @VincentChikopa-mm6ig
    @VincentChikopa-mm6ig 3 หลายเดือนก่อน

    Muuze bushili mon

  • @vitumbikochirwa2830
    @vitumbikochirwa2830 ปีที่แล้ว

    Enemies of progress.Bushiri is doing this for the betterment of the country. This is malawi property,bushiri is just engineering.its the government which is going to benefit

  • @squatmansaidi561
    @squatmansaidi561 ปีที่แล้ว

    Kkkk kma guys mawu awa akuyenera munthu wa ndemvu ku face

  • @tuntufyesichinga1071
    @tuntufyesichinga1071 ปีที่แล้ว

    Okay?

  • @phirisandfore643
    @phirisandfore643 ปีที่แล้ว

    Papa help me to change my life

  • @user-ng2nu6xn9x
    @user-ng2nu6xn9x ปีที่แล้ว

    AKADAKHALA KUTI ANTHU ENANSO AMAKHOBILI AKU MALAWI ALI NDI MOYO AKUONETSA A SHEPHERD BUSHIRI PANOPA MALAWI AKADAKHALA ATATUKUKA KOOPSYA

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 9 หลายเดือนก่อน

      Ndipo nzoona kunoku anthu ake ngansanje yauchitsilu nayo

  • @olipamaseko2693
    @olipamaseko2693 10 หลายเดือนก่อน

    Aaaa ndalamazi aaaa

  • @lonmediatech5864
    @lonmediatech5864 2 ปีที่แล้ว

    Iwe anthu azakumangisa.

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 ปีที่แล้ว

    No need of AcB because he z not apolitician

  • @fedinadisakala2380
    @fedinadisakala2380 2 ปีที่แล้ว

    Sanje amalawi musiyeni munthu atukulemalawi

  • @frankkamunde4575
    @frankkamunde4575 2 ปีที่แล้ว

    nsanje ndimene yakula nsinkhu

  • @MourinceNdaiyana
    @MourinceNdaiyana 7 หลายเดือนก่อน

    Wabodza iwe

  • @mustafailanga5010
    @mustafailanga5010 2 ปีที่แล้ว

    Sanje amalawi

  • @masiyekalisitusidayton9210
    @masiyekalisitusidayton9210 2 ปีที่แล้ว

    Apanga bwino nd2

  • @sidickbadat1086
    @sidickbadat1086 2 ปีที่แล้ว

    You have to screen this man the so called Prophet, whenever he got his money and how he made it, because this doesn’t look normal at all.

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 7 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @FacekidofficialmozMoz
    @FacekidofficialmozMoz ปีที่แล้ว

    🇲🇿Hi

  • @jonathandube9422
    @jonathandube9422 ปีที่แล้ว

    Bushili is a hill

  • @amosnyirenda5712
    @amosnyirenda5712 2 ปีที่แล้ว +1

    Zot zikuyenda chifukwa cha a Bushiri nde bodza the guy is bad luck kungobwera zinthu kuzsiiratu kuyenda kumalawi kuno. I dont like this guy

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 9 หลายเดือนก่อน

      Nchifukwa chake this country can’t go further because of sick and twisted people like you. If you don’t like him very good but don’t shit on whatever good thing he’s doing. And he didn’t ask you to like him or not. Tabakhalabe pa umphawi wakowo mfiti iwe

  • @patchipanga8445
    @patchipanga8445 2 ปีที่แล้ว

    Amange Malawi basi

  • @rasheedbanert7086
    @rasheedbanert7086 ปีที่แล้ว

    Zasatanic basi mboli yako iwe

  • @fridayngungadaud731
    @fridayngungadaud731 2 ปีที่แล้ว

    Channel ichi sindichikhulupirila anta

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 11 หลายเดือนก่อน

      Amaphatikiza choonadi ndi bodza vuto lake ndilimenelo

  • @bryanfuimaono709
    @bryanfuimaono709 ปีที่แล้ว

    you need to speak in English

  • @KAIPAAA3211
    @KAIPAAA3211 2 ปีที่แล้ว +1

    Wakuba wabela anthu ambiri ku south aafrica, amawanamiza anthu ambiri aike ndalama ku acount yake miez itatu apeza ndalama zambili ku ma count ao, ambiri akulila

    • @jomonor4915
      @jomonor4915 2 ปีที่แล้ว +2

      Dziko likufunika kukhala ndi munthu ngati uyu,uyutu amadzigwilila ntchito pa yekha wosati zomaba misonkho ya anthu.papa yr great wishing yu best mwatimasula amalawife

    • @saudamwanyali8700
      @saudamwanyali8700 2 ปีที่แล้ว

      Do you hv a proof for wat u a sayin

    • @ronaldchirwa253
      @ronaldchirwa253 ปีที่แล้ว

      Tazingogwirani ntchito apa... wakuberanipo chan chanu kapena cha makolo anu?

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 11 หลายเดือนก่อน

      Then akuba bwinotu coz he is stealing to help others