I support UTM and always i will miss SKC. Besides LUZ is the only president that malawi is currently having he deserves respect. If God can allow it that he should be distracted then we should know that the whole nation will be distracted. Rather let's pray that God should give great wisdom to those surrounding him because he is not a self decision maker. Am not condemning the song but comments that are flowing.
Komande atsekuratu mimba yoooo
Ndipo tiye nayeni sazaupeza m, tendele muthu opanda manyazi wamanga m,busa wa CCP lelolo akupita komweko umuthu alibe ndithu satana ameneu
😂😂😂😂
Ndiopepera Zedi ujaa😂😂😂
Mizimu yakwiya, waganiza zokapemphela lero, zaululika basi kuti black box yili ku state house., wanya.
Bodza ilo.
Mudziwerenga nkhani nokha ndi chifukwa chake ndinu a Misala
I support UTM and always i will miss SKC. Besides LUZ is the only president that malawi is currently having he deserves respect. If God can allow it that he should be distracted then we should know that the whole nation will be distracted. Rather let's pray that God should give great wisdom to those surrounding him because he is not a self decision maker.
Am not condemning the song but comments that are flowing.
Kkkkkkk koma kumeneko mulungu akhale nanu
Agonthi tilipo kumalawi CCAP sipanganawo zaukape mukamuona otelo nansongole ameneyo nyimbo yandale chuni chandale kuikamo yesu zipita kwina akhilisitu tisamale zandale ndiza yesu tiyense kupeza mayimbidwe athuathu
Its just asong nyimbo iyi ndiyakale imayimbidwa mostry in churches ostati chifukwa cha ndege no no no
Amen
Umunthu ngofunikadi munthu kumanga m busa wa CCAP lero mkumati mkupemphera komwe koma mzimu wa chilima uzuzadi anthu ndatha kuona tiyeni tipitilize kuyatsa makandulo mpakana Ambuye atiyankhe basi
Nyimboy ikugwirizama bwanji ndi chakwera sikukamba kalikose za chakwela mbuzi ukungofuna kuononga ma data aanthu
Kulikonse angapite kopephera nyimbo yake izikhala yoteroyo kuchitila kuti satana oyipayo azichita manyazi
Isshhh abwana alimavhuto ndithu
Bwanji osangowalola ena akaimire ku convention!😅😅😅😅😅😅
Koma ndikuona ngati munthuyu akhonza kungothawa!😅😅😅😅😅😅😅
Kkkkkkk....komatu achewa apa mwafika pena..😅😅😅😅😅😅...ndiye amanga ndani pamenepa? 😅😅😅😅😅😅😅
😂😂😂😂😂😂 Yomweyo Chikangawa sunati uzimangilira
Koma nde ayalukatu satana chokeledi akamwe magazi anthu 9 aja devil
Amen 🙏 🙏
Nde mumafuna kut ayimbe kuti yesu tichokere koma muli pa ntchito chakwera Ali phee
Mwamuchita bwino kumuimba satana opha anthu 9 amu Ndege
Ubwino wake mulibe dzina la munthu.
Komanso Chakwera sanachoke chothawa izo mwanama ife timali komweko.
Namizani a Misala enawa
Mulungu amuone agalu am kumumpha chilima Inu mulungu sangalole kuti muwine agaluiunu assatana
Munthu ukachita tchimo umakhala kapolo watchimolo.
M'zanu mukulimbana nayeyo sakukuyankhani zomwe mukupangazi mukupangitsa kt anthu mukuwanyozawa azingodalitsika bansi osachita mwanyazi kt palibe akukuyankha kd mukunjenjemete simunati
before 2025 General Election nkuruyu akhara atazimangilira
Anyanayo chakwera azipha ndithu
Mmmm zabodza koma athu eish
Sakudziwa kuti akutumikira satana yemweyo
Koma muli ndiganyutu kkkkk
Kkkkk km athu mwakwiya
Eyetu kwake kupha kuononga chikangawayo
Kkkkkkkk Koma kumeneko 😂😂
Koma zovuta kwabasi
Kkkķkk Chakwela ukuva bwanji?
Kkkkkk athawa sanatiii
😂😂😂😂😂Koma yaaah zoziputa 😂😂😂
Azimangilile satanayi
I think dis song it's not new one! It was present before
Funso ndiloti pa nyimbo zonse bwanji kungosankha iyiyi?
Yoo ziliko zafika pa mwana Akana phara ndithu bwanji manyazi
Wangwilo ndani?
Mbuzi za anthu aMCP kwathu Pena pake timati'agaru kunyindaa!"
Kkkkkk koma wina azipha chaka chake chino
😂😂😂😂😂😂😂😂 eeeish no comment on this hahahahahah
Amen ❤
😂😂😂😂😂😂😂
Kkkkkkkkkk 😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂
Muchedwa nazo izi
Zitizo zotchedwesa?
😂😂😂😂😂😂