Zoonadi wakuva akuva monga otsutsa
Ndikanakonda DPP, UDF, AFFORD akanabwera pamodzi ndikuyankhula za ma ID maka zomwe NRB ikupanga
Akuluu, asogoleli osusawa chomwe ndachiona ine ndichoti akuwopa kumangidwa ndikuphedwa nda mcp crocodile party 😂😂😂😂, funso mkumati akamawopa chomchi, amene awasogolele amalawi achokela kuti?, poti omwe timawatenga ngati m'busayu ndiuyu anayamba kutipha komanso kutikhamzikaka ndikutigoneka ndinjalayu.
Vuto ya zipani zotsutsa zikuyakhulira nyumba....sizikufuna kubwela poyera mkuima pa mbalambanda mkuyakhula angoti ziii sopano anchinyamata akufuna mtendele atulukila bwanji poyera....opposition rising up
Chakwera kudzangowina basi ngakhale otiyankhulira alerowa sadzapezekaponso ndithu chifukwa ma warning ndiye tikulandiliratu koma no any action is taken
PDP ichotseni ndi ya Ku tonse alliance.
Ngati amtsogoleri a DPP, Aford, utm ndi zipan zina sayakhulapo zimenezi,, adziwe kuti ife timuika mokakamiza boooooooon kalindo
Action ndiyomwe imafunika koma aMalawi ife ndizitsilu timangoyang'anira zinthu zikuonongeka
Komanso kodi a kalindo ndianzanu simungangoyambitsa chipani chanu mudzitsutsa bwino
Kuyankhula ndiye anthu akulankhura ndipo zowona zokhazokha koma zipani zosusa zangoti ziiii basi kaya chifukwa chani mmadera ambili anthu sanalembese
Munthu amene anali osaopa ndi kusunsa anali malemu Mr chilima
Amwene mwalankhulana zomveka ndipo ine ndagwirizan nazo,zoti povota tisazagwiritse ntchito ID
Nkhani ndiyoti tisazagwilise mavoti pokavota, tizangovota ngati momwe tinavotera 1994 opanda chawumzika , ndipo izi kuti zitheke zikufunika asogoleli osusawa kupita ku court akasume komanso a law society apangepo kanthu pankhaniyi, koma vuto ndiloti mabungwe onse omwe amayenera kumaima pawokha pano alimunkhwapa mwa crocodile party
,Amayi dzikomo kwambiri chifukwa cholikonda dziko lathu ndiponso powadzutsa azipani zotsutsa a Malawi tichenjere chifukwatu chakwera ndi kathyali
Nzimenezo ndidzoona kupanda kusamala chakwela kungolowa Boma tiziwe Kuti tidzankhala muukapolo
Ma ID akhasulidwe tikavote basi.
Zoona ma leaders a opposition wake up from the your deep slumber start preparing for the election coming soon nonse otsutsa kharani pamodzi nthawi yatha mcp sikugona🎉
Ma opposition a Ku malawi ndi ogona...ndi MCP yokha imene inali ya jack up...Ali Ku opposition...zachamba basi
Kuyankhula kwabwino ndithu munthu wankazi
ID Isagwilitsidwe Ntchito povota ambiri ife tilibe ID, koma tikufuna kuzavota ndiye ichosedwe system yovotera ma ID aliyense azizangovota basi
Kkkkkk zoona achakwela ndi muthu woyipha kwambili zavura zamuthu ayi
Kodi kumalawiko kunayamba kwa khala opposition? Kodi a Tupele muluziyo kuti adzipezeka m'boma zinakhala bwanji? Chifukwa kunena zowona malankhulidwe pena pake amafotokoza m'mene munthu aliri.
We are ready here in Lilongwe, mademo ayende basi
Mau Mau Mayi.....Ndikhulupira kuti Opposition yathu inva.zimenezi
Tivotera chakwera yemweyo ndi mcp chifukwa ndi chipani ziko osat za kubanja zija,olo kut afe peter leloli nde kut akatengaso mwana wa bingu ,kukanfunafuna kut mpaka nayeso azakhale president
A law society komanso a mec onse angokhala pheee , kumangowonelela zinthu zikulakwika mudziko lathu , nkhani ndiyoti anadya ndalama zamisonkho yathu akafucheche amenewa
Tikudabwa anthu angati chetee sakuyankhula azipaniwa ndi mabungwe tinganene kut akuopa?amenewadi asadzatinyanse otsutsawa akadzawa bela kut tiyeni pansewu.akugona okha otsutsawa even wachiwili otsutsa boma aliphee kupaliuament osayankhula adzalira amenewa mwina sakufuna u president.
Palibe kuvota nd id
tivota opanda chazika
Tafika bwana
Kodi ndee inu a opposition zinthu zimene zimakambidwaziii simavera ?
Chakwera akuchepera kaba zisiteka kuwinaso ayi athu aganisazoso mwachangu zoona madam
Muone kuti osusa ndiogona ndi izi ku mzuzu blantyre mangochi ma ID ma passport anasiya kupanga zose zikupangidwa ku lilongwe komwe kuli mcp please sekulani maso osusa.
Zoonadi Ma lD yavutadi .Tisadzagwilitse ntchito ma id Chonde eeeeeeeee
Mai mukunena zoona ineyo ndinanena kale kuti ngati mcp izawine 2025 amalawi ambiri adzavutika. Ndipo mazuzo aka adzaposa amene tikuganiza akubaga moyo
Where are the fuckin opposition in Malawi, mulikuti makapenu zinthu azikuyankhulilani anthu zoona??? Like seriously???
Ndizoona ndithu okuva ave chonde dzuka malawi
Mukunena zoona amayi
Zoonad zimenezo
Ndipo izi ndie zoonadi
Zoonadi izi
Zoona dzuka malawi
Amalawi tiyen tidzuke tisalore kut chakwera 2025 alowenso m'boma
Mbambande zedi ndithu ❤❤❤❤ guys lamuro la ID tisazaloreyi, aliyense azizangovota basi
Simudzalora motani? Muuzeni amene watumiza audio-yi kah kut ndiye tizatanii osati azingoyankhula without solution
@@isaacchiwaula731 Tati sitizalora coz ndiufulu wathu ovota ndipo tizavota osagwiritsa ntchito ma ID coz tonse ndi mdzika
Chilungamo kwambiri chemwali.
Opposition parties wake up and go to courts seek for justice.
Stop this ID protocol while it's too early
Kuyambilakalekale sitimavotela chaunzika ayi ndipozimenezo sizizathekaayi tizavota mmenetimavotela zakazonse
Ma ID akhasulidwe tikavote basi.
Osati tsoka akulu dziko muziyenda nalo atsutsa akuno Ku Malawi sangawine musabvuti ai ndiokulilana mtima
Mukunena zoona mayi.
Ma opposition party mukumumva mzimaiyu kkkkkk Kodi mukukhalangati akuikani mmbotolo bwanji