ความคิดเห็น •

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 3 วันที่ผ่านมา +1

    Ma opposition party mukumumva mzimaiyu kkkkkk Kodi mukukhalangati akuikani mmbotolo bwanji

  • @kurhikhoza8298
    @kurhikhoza8298 2 วันที่ผ่านมา +1

    Zoonadi wakuva akuva monga otsutsa

  • @sylvesteralfred8355
    @sylvesteralfred8355 3 วันที่ผ่านมา +10

    Ndikanakonda DPP, UDF, AFFORD akanabwera pamodzi ndikuyankhula za ma ID maka zomwe NRB ikupanga

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 3 วันที่ผ่านมา

      Akuluu, asogoleli osusawa chomwe ndachiona ine ndichoti akuwopa kumangidwa ndikuphedwa nda mcp crocodile party 😂😂😂😂, funso mkumati akamawopa chomchi, amene awasogolele amalawi achokela kuti?, poti omwe timawatenga ngati m'busayu ndiuyu anayamba kutipha komanso kutikhamzikaka ndikutigoneka ndinjalayu.

    • @GospelSoldiers-sr7np
      @GospelSoldiers-sr7np 3 วันที่ผ่านมา

      Ndipo kwambili akuyenera kusamala

  • @user-em1qi8kj9h
    @user-em1qi8kj9h 2 วันที่ผ่านมา

    Vuto ya zipani zotsutsa zikuyakhulira nyumba....sizikufuna kubwela poyera mkuima pa mbalambanda mkuyakhula angoti ziii sopano anchinyamata akufuna mtendele atulukila bwanji poyera....opposition rising up

  • @sylvesteralfred8355
    @sylvesteralfred8355 3 วันที่ผ่านมา +9

    Chakwera kudzangowina basi ngakhale otiyankhulira alerowa sadzapezekaponso ndithu chifukwa ma warning ndiye tikulandiliratu koma no any action is taken

  • @user-jw5rx9ze8k
    @user-jw5rx9ze8k 3 วันที่ผ่านมา +3

    PDP ichotseni ndi ya Ku tonse alliance.

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o 3 วันที่ผ่านมา

    Ngati amtsogoleri a DPP, Aford, utm ndi zipan zina sayakhulapo zimenezi,, adziwe kuti ife timuika mokakamiza boooooooon kalindo

  • @sylvesteralfred8355
    @sylvesteralfred8355 3 วันที่ผ่านมา +6

    Action ndiyomwe imafunika koma aMalawi ife ndizitsilu timangoyang'anira zinthu zikuonongeka

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 3 วันที่ผ่านมา

    Komanso kodi a kalindo ndianzanu simungangoyambitsa chipani chanu mudzitsutsa bwino

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula ndiye anthu akulankhura ndipo zowona zokhazokha koma zipani zosusa zangoti ziiii basi kaya chifukwa chani mmadera ambili anthu sanalembese

  • @user-mo5od8cy3n
    @user-mo5od8cy3n 2 วันที่ผ่านมา

    Munthu amene anali osaopa ndi kusunsa anali malemu Mr chilima

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 3 วันที่ผ่านมา

    Amwene mwalankhulana zomveka ndipo ine ndagwirizan nazo,zoti povota tisazagwiritse ntchito ID

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 วันที่ผ่านมา +2

    Nkhani ndiyoti tisazagwilise mavoti pokavota, tizangovota ngati momwe tinavotera 1994 opanda chawumzika , ndipo izi kuti zitheke zikufunika asogoleli osusawa kupita ku court akasume komanso a law society apangepo kanthu pankhaniyi, koma vuto ndiloti mabungwe onse omwe amayenera kumaima pawokha pano alimunkhwapa mwa crocodile party

  • @anifoiuene6301
    @anifoiuene6301 2 วันที่ผ่านมา

    ,Amayi dzikomo kwambiri chifukwa cholikonda dziko lathu ndiponso powadzutsa azipani zotsutsa a Malawi tichenjere chifukwatu chakwera ndi kathyali

  • @user-hx6ly3cl8m
    @user-hx6ly3cl8m 3 วันที่ผ่านมา

    Nzimenezo ndidzoona kupanda kusamala chakwela kungolowa Boma tiziwe Kuti tidzankhala muukapolo

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 วันที่ผ่านมา

    Ma ID akhasulidwe tikavote basi.

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 3 วันที่ผ่านมา +1

    Zoona ma leaders a opposition wake up from the your deep slumber start preparing for the election coming soon nonse otsutsa kharani pamodzi nthawi yatha mcp sikugona🎉

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 3 วันที่ผ่านมา +1

    Ma opposition a Ku malawi ndi ogona...ndi MCP yokha imene inali ya jack up...Ali Ku opposition...zachamba basi

  • @user-nr1xo1nw3z
    @user-nr1xo1nw3z 3 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula kwabwino ndithu munthu wankazi

  • @John-to8gl
    @John-to8gl 3 วันที่ผ่านมา

    ID Isagwilitsidwe Ntchito povota ambiri ife tilibe ID, koma tikufuna kuzavota ndiye ichosedwe system yovotera ma ID aliyense azizangovota basi

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 3 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkk zoona achakwela ndi muthu woyipha kwambili zavura zamuthu ayi

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 3 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi kumalawiko kunayamba kwa khala opposition? Kodi a Tupele muluziyo kuti adzipezeka m'boma zinakhala bwanji? Chifukwa kunena zowona malankhulidwe pena pake amafotokoza m'mene munthu aliri.

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y 3 วันที่ผ่านมา +1

    We are ready here in Lilongwe, mademo ayende basi

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 3 วันที่ผ่านมา +1

    Mau Mau Mayi.....Ndikhulupira kuti Opposition yathu inva.zimenezi

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 3 วันที่ผ่านมา

    Tivotera chakwera yemweyo ndi mcp chifukwa ndi chipani ziko osat za kubanja zija,olo kut afe peter leloli nde kut akatengaso mwana wa bingu ,kukanfunafuna kut mpaka nayeso azakhale president

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 วันที่ผ่านมา +1

    A law society komanso a mec onse angokhala pheee , kumangowonelela zinthu zikulakwika mudziko lathu , nkhani ndiyoti anadya ndalama zamisonkho yathu akafucheche amenewa

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 วันที่ผ่านมา

    Tikudabwa anthu angati chetee sakuyankhula azipaniwa ndi mabungwe tinganene kut akuopa?amenewadi asadzatinyanse otsutsawa akadzawa bela kut tiyeni pansewu.akugona okha otsutsawa even wachiwili otsutsa boma aliphee kupaliuament osayankhula adzalira amenewa mwina sakufuna u president.

  • @EDGARKADZAKUMANJA
    @EDGARKADZAKUMANJA 3 วันที่ผ่านมา

    Palibe kuvota nd id

  • @FunnyKalimwayi
    @FunnyKalimwayi 3 วันที่ผ่านมา

    tivota opanda chazika

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 วันที่ผ่านมา

    Tafika bwana

  • @JumaKachala
    @JumaKachala 3 วันที่ผ่านมา

    Kodi ndee inu a opposition zinthu zimene zimakambidwaziii simavera ?

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt 3 วันที่ผ่านมา

    Chakwera akuchepera kaba zisiteka kuwinaso ayi athu aganisazoso mwachangu zoona madam

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 3 วันที่ผ่านมา

    Muone kuti osusa ndiogona ndi izi ku mzuzu blantyre mangochi ma ID ma passport anasiya kupanga zose zikupangidwa ku lilongwe komwe kuli mcp please sekulani maso osusa.

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 3 วันที่ผ่านมา

    Zoonadi Ma lD yavutadi .Tisadzagwilitse ntchito ma id Chonde eeeeeeeee

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 3 วันที่ผ่านมา

    Mai mukunena zoona ineyo ndinanena kale kuti ngati mcp izawine 2025 amalawi ambiri adzavutika. Ndipo mazuzo aka adzaposa amene tikuganiza akubaga moyo

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz 3 วันที่ผ่านมา

    Where are the fuckin opposition in Malawi, mulikuti makapenu zinthu azikuyankhulilani anthu zoona??? Like seriously???

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh 3 วันที่ผ่านมา

    Ndizoona ndithu okuva ave chonde dzuka malawi

  • @user-hg8zy8pt5b
    @user-hg8zy8pt5b 3 วันที่ผ่านมา

    Mukunena zoona amayi

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 วันที่ผ่านมา

    Zoonad zimenezo

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 3 วันที่ผ่านมา

    Ndipo izi ndie zoonadi

  • @ThomasHandson
    @ThomasHandson 3 วันที่ผ่านมา

    Zoonadi izi

  • @Rose-wu5ef
    @Rose-wu5ef 3 วันที่ผ่านมา

    Zoona dzuka malawi

  • @user-gx3xc9lk8x
    @user-gx3xc9lk8x 3 วันที่ผ่านมา

    Amalawi tiyen tidzuke tisalore kut chakwera 2025 alowenso m'boma

  • @user-ji5gq4cf6r
    @user-ji5gq4cf6r 3 วันที่ผ่านมา

    Zazii. Vuto ndi lakuti ma boma ambuyo akhala akubwera mavoti

    • @Zelinakhisswell
      @Zelinakhisswell 3 วันที่ผ่านมา

      Nde bwezi akuchoka pa mpando 😅

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 3 วันที่ผ่านมา

    Mbambande zedi ndithu ❤❤❤❤ guys lamuro la ID tisazaloreyi, aliyense azizangovota basi

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 2 วันที่ผ่านมา

      Simudzalora motani? Muuzeni amene watumiza audio-yi kah kut ndiye tizatanii osati azingoyankhula without solution

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 2 วันที่ผ่านมา

      @@isaacchiwaula731 Tati sitizalora coz ndiufulu wathu ovota ndipo tizavota osagwiritsa ntchito ma ID coz tonse ndi mdzika

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 วันที่ผ่านมา

    Chilungamo kwambiri chemwali.
    Opposition parties wake up and go to courts seek for justice.
    Stop this ID protocol while it's too early

  • @JosephMwambe-rz2oy
    @JosephMwambe-rz2oy 3 วันที่ผ่านมา +2

    Kuyambilakalekale sitimavotela chaunzika ayi ndipozimenezo sizizathekaayi tizavota mmenetimavotela zakazonse

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 วันที่ผ่านมา

    Ma ID akhasulidwe tikavote basi.

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 วันที่ผ่านมา

    Osati tsoka akulu dziko muziyenda nalo atsutsa akuno Ku Malawi sangawine musabvuti ai ndiokulilana mtima

  • @EagerChicken-qj6xu
    @EagerChicken-qj6xu 3 วันที่ผ่านมา

    Mukunena zoona mayi.