Manganya ndi bambo a sikono tisaiwale pamepo. Ndipo ndi mthila kuwili kapena chidule chadzina nale ndi chikakha manyi chomatuluka thukuta koma chikukakha zonukha ndiye ndi manganya
Manganya akuchita kuyamikila poyela ATI chakwela anampasa y VP manganya ndiwa MCP koma choti aziwe nduchakut kuli achina zikhale ng'omaa Abid Mia ambili mbiku akuufuna u vice president umenewo Atamuonese show ndi achina zikhale imwewo osat chakwela
Bamboake a sikono ndi khwangwala ozola Ufa oyera kuti afanane ndi akakowa oyera kobadwanako . Koma powoloka pamazi azaziwika kuti bambo sikono ndi khwangwala.
Koma manganya wakhumudwitsa athu sakuchita bwino ndipo ndimkamukonda ndimkaona ngati masewelo anha ndiwadzelu kani ndiwachabe Chomcho mm wampeleka nzake koma mmm ndiolotse ndikakutafune Ambuye atithandize ndithu
Manganya ndi wa MCP umbon lowani ku FB kuli movie ya manganya act same like kamudzu banda this is a true
manganya akuwona ngati angapusise anthu akunama imfa ya achilima manganya akuziwapo kathu chakwera ndi chigawenga
A Miko usi zomwe zimakukhalani ndi ma drama osati ndale mwalowa mbali yolakwika muyaluka😂😂😂😂
Zomwe zikuchikazi, ndikupanda Mzimu waumunthu komanso Kusowa chochita.. Kodi zinthuzi anganamizidwe ndindani ngati a Malawi sitikudziwa ayi ayi ,auponda Mr DJ don't trust.
Manganya atumikila MCP APITILA limodzi ndi MCP yakoyo 2025
Zimvere mumtolo manga we proud of you Limpopo guys
Misonkho yathu yomwe lero kumatikongoza mwauponda anthu adya zimenezo koma osabweza😂😂
Ndipo inu 😂😂😂
Asiyeni nthawi yawo atipeza pompano nthawi nkachisilu
Komaso olo apileke ngongole panopa zaka zonsezi anali kutiko ndiye akuwona ngati angatipusinse ife mapwala ake manganya chisiru
Ndalama aba iba athu oipa asatana manganya naye aferazayen
Bweresani ngongoreyo tikagulire chakudya njala bwana kuno
Manganya ndi bambo a sikono tisaiwale pamepo. Ndipo ndi mthila kuwili kapena chidule chadzina nale ndi chikakha manyi chomatuluka thukuta koma chikukakha zonukha ndiye ndi manganya
Kungotengela khalidwe lake olo patakhala pasewelo emwa ama ima pa zaphindu ndi winiko. Kusonyeza awawa kaumuthu alibe koma kupusitsa ena basi.
Manganya ndi yemwe amamupereka chilima, koma mulungu simuthu mawa mawali ndi iweyo
Manganya ndamene apeleka Chilima komaso ndi wa MCP.
Manganya ndi wa mcp kuyambila kale kale ndipo za chilima waphesa ndi iyeyi
Awulutse maviyen anthu awuze okuphawo
Ndi waku Zimbabwe ameneyu si mmalawi
MCP you mast ❤
Mwana akalakwa timamukwapula manganya ndi mwana ayenera kukwabulidwa ngati mwana
Manganya manganya manganya.Amalawi ochuluka akutuluka.akungokunamiza amenewo
manganya muthu oyipa ngati mutchimbuzi
Manganya akuchita kuyamikila poyela ATI chakwela anampasa y VP manganya ndiwa MCP koma choti aziwe nduchakut kuli achina zikhale ng'omaa Abid Mia ambili mbiku akuufuna u vice president umenewo
Atamuonese show ndi achina zikhale imwewo osat chakwela
Anthu9 ose anaphedwa osalakwa kuchikangawa ndipo amene amakaulaura zisisi zachilima ndiyemweyu Kwa chakwera izi ndi imfa zimene sizizaiwalika komaso Ife ovota sitingaiwale.komaso adziwe Kuti palibe wamyaya padzikolino nawoso alipaulendo adzafa Chuma ngakhale achikonde bwanji Koma Azachisiya
Limpopo ndimakusatani koma whatsapp line ndilibe, nane ndiziponyako maganizo anga plz.
Nsonda anabadwa Ali otuwa akukula Ali otuwa azafanso Ali otuwa ndimulomo wake wautali ngati sakhwi.
Koma manganya akuwona ngati angatinamize ife akunama iyeyo ndifiti yake ckwalelayo
Manganya ndi wa Mcp! Koma sangatiuze china chilichose
Akeni sonda I think amwa mankhwala thawi yaitali ndiye mutu unasiya kugwila ntchito
😂😂😂😂😅😅😅 akufunika akamusinthile mankwala 😅😅😅😅😅@@MilikaKilion-tn1bn
Manganya ,,,why ? Sakuvala makaka a UTM fotseke ameneyo achoke muchipani cha UTM ,,, Kodi zomwe akupanga manganya sika mpeni bwanji asonda akudana ndi fedokisi Kuti asiye makendulo ,,zitsilu zawanthu Za MCP. ,,,manganya akabwela tawuni yakwanthu tidzangenda ayelekeze
Zoona zake
Amanganya anthu akukuwelengani pang'opang'ono koma anthu akukusatirani kamba ka UTM mubwere poyera kuti ndi WA MCP muone zomwe tichite PA nchombo wako
Za Ken Msonda whether wakula kaya watani akungofunika kulanga ndi makofi simple
Zakukulako ziri apo athibulidwe basi ndi opisa
Bambo a Nick ndi Bambo a Sikono magazi a chirima ayamba kuwapengesa misala. Ayamba kusavuka .
Manganya angoyenda mwantendele ku mcp akamuphele konko
Bamboake a sikono ndi khwangwala ozola Ufa oyera kuti afanane ndi akakowa oyera kobadwanako . Koma powoloka pamazi azaziwika kuti bambo sikono ndi khwangwala.
Limpopo umakwana
Manga akupanga kampen watumidwa zonse zomwe achita yankho ilipo 2025 ndipamene aziwe kut malawi walero siwathawi ya kamudzu tiwakhazika pansi 2025
Mavotedwe aliyense akuyenela avote kugwirisa pepala iliyonse yochoka kwa amfumu
Hello Don't trust. Big up
Akupanga zachamba manganya
Asapusitse amalawi kawiri akakupatsani ngongoleyo idyani ndalamayo ndipo musabweze chifukwa ndi misonkho yanu
Manganya alibe zelu
Manganya ndi galu wamuthu anachenjeletsa mopusa ine ndipo amandinyasa kwambili ndipo sitingavitele zitsilu zimenezi
Manganganya ndiwa MCP patalike pafupike uyaluka manganya 2025 athu akumpha inu
Manganya ndi joker,anachenjera mopusa akuona Ngati amalawi ndi opusa kuti atsatira maganizo ake, ndalama anthu apatseni komanso olo osabwenza palibe milandu potion AMAT wadya zake alibe milandu ndi ndalama zathu zija
Program yowophya ku chipani cha chakwera osayisiya avesese
Tikhoza kukamba kuti amakaoda akapeleke ku mwela akagawe kwa mtundu wa Malawi
Manganya u mast go
Koma ndiye galu osaka weniweni
Ndi 1
Chakwera wakugwirisa ntchito manganya
Vuto chilima sanaziwe kuti manganya ndi udasi manganya si wa utm asatinamize manganya zeru walibe akuyendera zipatala koma mankhwala mulibe koma akugawa mhongole kwa anthu oti ali bwino alibe vuto koma kuzipatala kulibe mankhwala anthu akumwalira pali zeru panenepo. Ine ndikanakhala manganya ndikanamuwuza Chakwera kuti asiye kukongoza ndalama ndalama zo akagule mankhwala
Usi Ndi munthu oipa kwambili
.
Ndalamazo zidyedwe koma vote Ili mumtima
Athu oipa awa nasatana awamako mwandi
Manganya manganya manganya.Amalawi ochuluka akutuluka.akungokunamiza amenewo
Ndipo sakuwaziwa