The only wise and rational person who leaves a beautiful place where everything is going well and goes to live with the people who are suffering,will find favor in the presence of the almighty God.
Whether the votes will be minus 20% we don't care . USI and the cabinet ministers can remain at MCP we don't care .The best Usi can do is to start his party and do the alliance with MCP . That will be his correct decision. He must not use UTM emblem because at UTM I don't see his impact achedwa kwambiri.
Programe iyi kulibwino angoyithetsa chifukwa zimene zimakambidwa akumapanga back up mcp so palibe Amalawi yingatithandize Programe yanuyi ayi just suspend it
Kodi chawezi yu mumamutengelanji? Uyuyu adzandilakwitsa one day. Victor or abel, banda are the bes uyu ndiwa mcp. Sadzatheka Chawezi akupeza zabwino ku bomaku ndipo ativuta kulera 😅
Chaweza what you should know is we didn't do a hasty decision . It a fine a decision and you can't change it. We are not desperate rather and we as voters cannot take it Chawezi you are MCP and no body can listen to your views . Member wa nzeru cannot proceed to be in alliance with MCP .
Ngati Dewesi ali pa banja njofunika kumunyengera mkadzi wake nde kupanga dzoti anthu adzamugwire mkadziyo akuchita chigololo nde iyeyo adzamve, then tidzaone ngati adzadekhe osathetsa banja antil 3 months
Mbuzi Chawezi
Iweyo tangopanga Za MCP yakoyo usalimbane ndi UTM
Mesa inu a MCP ndamene mwamupha Chilima
Nde chokhalira mu mgwilizanomo ndichani?
Chawezi ndiwe mbuzi kwambili
Ndiwa Mcp uyu, anthu mwawaphera mtsogoleri akhalebe komko
It's a move by DPP and they have allowed kabambe to be leader in order to redirect all UTM followers back to DPP
Mgwirizano unatha kale mu 2020 kadasala ndikutulukaku☝️
Iwe chawezi president ananena poyera kuti ayima in public mzake ali pomwepo mmmmm ine si wandale koma mzeru mzako ndi zofoka kwambir
This chawezii he's MCP member
Achewa alibe respect ndipo ndiwophangira kwambiri, utm yachita bwino
The only wise and rational person who leaves a beautiful place where everything is going well and goes to live with the people who are suffering,will find favor in the presence of the almighty God.
Komaso muthu akamwalila pamabeera wina basi
Tikuyenela kumapephela tsiku ndi tsiku, nthawi ndi nthawi chifukwa satana ndiwochenjela atha kutigwesa m'mayeseli
Zomwe adagwilizana chilima adanena pa press briefing kt ndi 5/5 ndy inu mukut anadziwana awili bwanji
A Chawezi kunali amzathu , muzatha mosakhala bwino
Palibe
Nkhani apa...ngwilizano unatha ...adekhe why?
Mbuzi iwe chawezi mafuta sangatchipe kuno iwe galu iwe usadandaule ukhala wankulu wa MBC galu iwe
Chawezi palibe zodekha MCP is helpless to UTM. What you should focus is MCP agenda
Mabwana a chawezi tamuchoseni uyu pa program imeneyi, we need balanced issues, awa ndi achibwana, a Mbuye Mulungu wa zonse mkatheni chawezi yu amen
Kaliat ndi kathyali nfiti yaikaz
Sanalakwise chifukwa zomwa adagwilrizana mungwilizano wawo palibe akuziwa
Nkona anamuxhotsa ntchito ku mbc uyu xhitsiru wamva
Palibe chifukwa cholembela kalata yothela ubalewawo nde asadijile kalata kodi mr chikangawawo atava zimezi anayitanapo a UTM kuti akambilane zakutuluka kwa UTM? Zomatiseka kumaso uwe chawezi uzingodya misokho ya amalawyo osatipusisa mene munkapanga zachipongwe ndichilima ndemumati atani palibeso zodikila myezi mafuna mugule UTM yose nde mwauponda mwakumananazo zanadulila muwona nyekgwe a MCP muwuzeni chimwendo abeleke over muzapenge gwilizano ndi ana achimwendo
Ndipo monga ngati ine ndikuti anakhonza kwambili kutulukako mcp down
Timafikila kuti chilima atiyakhule poti wamwalira a Patricia watiyakhula
Ayi choka iwe chawezi utm yachitabwino kutuluka musanga kt akozenyumba yawo even chilima akanavela kalindo bwezi izi kulibe lero winiko amanena zoona kt tulukani mu tose koma sanavele
Utm yagulisa chipani ku dpp
Chawezi umatha
Kuchoka mungwilizano kwachitika munthawi yake
Chawezi great analysis
Ndipo achawezi sawlekeze kuonesa mutu ukakwela galimoto yako tikukhazula tionana aise manyi ako wanva
Chisilu iweyo simadziwa Kuti Pali ndale kupha chilima
Satana akalowa mpovuta kumutulusa, Chawezi amlowa satana.
Chawezi capaign director wa mcp banja likatha palibe za ulemu
Or ndi dzina lomwelo likungosonyeza kut ndi wa MCP
Chawezi ndi wa MCP
Pamtumbo panu inuyo mwasowa zokamba mamwapwala anu
Ngati, mgwirizano unali wa anthu awiri basi uthepo winayo anatisiya ndiye UTM isiyeni
Chawezi ndiwe Galu
Whether the votes will be minus 20% we don't care . USI and the cabinet ministers can remain at MCP we don't care .The best Usi can do is to start his party and do the alliance with MCP . That will be his correct decision. He must not use UTM emblem because at UTM I don't see his impact achedwa kwambiri.
Chawedzi ndiwe osokonedza
Kod iweyo why ukukamira zimenezo ndiwe mbuzi et ?
Iwe apanga nthawi yoyenera, afufuza bwanji za ifa ali ku tonse komweko? Aasa!
Chawezi zinarakoro ndiramunthu wamukazi anakupasayo anakuwononga ndiye utisamare uzapezeka mumavuto mumene umamwera mowa iweyo🆗
Agalu inu
Programe iyi kulibwino angoyithetsa chifukwa zimene zimakambidwa akumapanga back up mcp so palibe Amalawi yingatithandize Programe yanuyi ayi just suspend it
Kodi chawezi yu mumamutengelanji? Uyuyu adzandilakwitsa one day. Victor or abel, banda are the bes uyu ndiwa mcp. Sadzatheka Chawezi akupeza zabwino ku bomaku ndipo ativuta kulera 😅
Chawez u hv no timing
Chawezi samalira ayise we know ukulimbana ndi azipani zotsutsa samalira ayise I know you are there for mcp
Chaweza what you should know is we didn't do a hasty decision . It a fine a decision and you can't change it.
We are not desperate rather and we as voters cannot take it
Chawezi you are MCP and no body can listen to your views .
Member wa nzeru cannot proceed to be in alliance with MCP .
Useless program
Achilima anali odekha mtima, koma ku bwela kwawo ulendo wakunja uja koria,anali ndicholinga chotuluka mu tonse kale, koma tsoka asanaphume kubwela kwaku koria ,ndimene amapita kumarilo akusambala posadziwa kuti awusi chisisi anakamuuza kale chakwela, kodi zonsetu tikuzidziwa koma ndalama ndalama, koma mulungu simuthu
UTM IS NOT THE FIRST PARTY TO MOVE OUT OF THIS ALLIANCE , PEOPLE ARE TALKING ALOT BECAUSE IT HAS MANY YOUTH FOLLOWERS SO ZIKUBAYA ANTHU AMBIRI.
Where is victor
Chawezi uzafa ngati garu
Chawezi umawoneselatu kuti ndiwe wa MCP all times on this program
In life ngati mkazi wakukana olo mutalankhula motani it's helpless to the man.
UTM is done with MCP
DK simunthu wamba UTM ikutenga boma 2025
Ngati Dewesi ali pa banja njofunika kumunyengera mkadzi wake nde kupanga dzoti anthu adzamugwire mkadziyo akuchita chigololo nde iyeyo adzamve, then tidzaone ngati adzadekhe osathetsa banja antil 3 months
Chawezi ndi wa chakwera
Chawezi chawezi chawezi
we don't like Chawezi on this Program
Ulemu wa chani galu iwe chawezi, umamupasa ulemu munthu oipa
Miyezi 4 inachuluka anthu ambiri akanasala ku mcp , achita bwino kutuluka fumbi la kuchikangawa lisanathe .
Komatu chawedzi pena amayankhula ngati mbuli zedi kodi amene samadziwa kuti alliance ya utm ndi mcp inali yoti five yrs wina akhala president kenako wina azaimeso, ndi chifukwa ichi ndi chomwe chinabwelesa kusagwilizana cz ingakhale Dr late SKC ananena poyera kuti ngati Dr chakwera sakufuna kutula pansi udindo ndiye tiyenera tikavote. Utm kutuluka siinalakwise aii cz mcp siinalemekedze ingakhale imfa ya chilima mzinthu zambiri kumapanga msonkhano anthu akulilabe kenako uziti afulumira kutuluka ukhalike ndithu ngati akukunyemera tazingodya makobidiwo komano usaganize mombwambwana aiii
Ine anthu awa amandionekera mwa mcp cp eeee ndiye aaaa sinkonda kunvera zamenewa
Chawez ndi iwe mbuzi
Chawezi wabodza iwe, sukuyenera kukhara analysis poti zuonekeratu ndiwe wa MCP
He knows only how to speak but not to understand what he is speaking. Mr Chawezi 😅
Ndi ntchito yawo,,,anali kuti? Nthawi yonseyi
Halayansi yabayatu
Zinthu zake
Wabweza bwanji?
Unuso mukuziwa mugwilizano panalibe
Zoonad iwe
Ineyo i don't like this guy is not the best for me ........
Chawezi ma comments ako ngooneseratu uli mbali yinayo uli against UTM