KWACHEMA KUBWEZA MOTO CHAWEZI |

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 6 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 76

  • @momuumro
    @momuumro หลายเดือนก่อน +11

    Mbuzi Chawezi
    Iweyo tangopanga Za MCP yakoyo usalimbane ndi UTM
    Mesa inu a MCP ndamene mwamupha Chilima
    Nde chokhalira mu mgwilizanomo ndichani?
    Chawezi ndiwe mbuzi kwambili

    • @JustinLipipa
      @JustinLipipa หลายเดือนก่อน

      Ndiwa Mcp uyu, anthu mwawaphera mtsogoleri akhalebe komko

  • @aaronziyeretsa6420
    @aaronziyeretsa6420 หลายเดือนก่อน

    It's a move by DPP and they have allowed kabambe to be leader in order to redirect all UTM followers back to DPP

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo หลายเดือนก่อน +3

    Mgwirizano unatha kale mu 2020 kadasala ndikutulukaku☝️

  • @user-qz1rp5mh9e
    @user-qz1rp5mh9e หลายเดือนก่อน

    Iwe chawezi president ananena poyera kuti ayima in public mzake ali pomwepo mmmmm ine si wandale koma mzeru mzako ndi zofoka kwambir

  • @HeinzeVictorMumbai
    @HeinzeVictorMumbai หลายเดือนก่อน +4

    This chawezii he's MCP member

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 หลายเดือนก่อน

    Achewa alibe respect ndipo ndiwophangira kwambiri, utm yachita bwino

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน

    The only wise and rational person who leaves a beautiful place where everything is going well and goes to live with the people who are suffering,will find favor in the presence of the almighty God.

  • @Brihippo
    @Brihippo หลายเดือนก่อน +1

    Komaso muthu akamwalila pamabeera wina basi

  • @JohnFrank-cg1yh
    @JohnFrank-cg1yh หลายเดือนก่อน

    Tikuyenela kumapephela tsiku ndi tsiku, nthawi ndi nthawi chifukwa satana ndiwochenjela atha kutigwesa m'mayeseli

  • @user-sm6pr9cg2q
    @user-sm6pr9cg2q หลายเดือนก่อน

    Zomwe adagwilizana chilima adanena pa press briefing kt ndi 5/5 ndy inu mukut anadziwana awili bwanji

  • @godfreyamos7452
    @godfreyamos7452 หลายเดือนก่อน +1

    A Chawezi kunali amzathu , muzatha mosakhala bwino

  • @MAYAMIKOCHALIRA
    @MAYAMIKOCHALIRA หลายเดือนก่อน +2

    Palibe
    Nkhani apa...ngwilizano unatha ...adekhe why?

  • @mbelengamavuto2517
    @mbelengamavuto2517 หลายเดือนก่อน

    Mbuzi iwe chawezi mafuta sangatchipe kuno iwe galu iwe usadandaule ukhala wankulu wa MBC galu iwe

  • @DysonUmali
    @DysonUmali หลายเดือนก่อน +1

    Chawezi palibe zodekha MCP is helpless to UTM. What you should focus is MCP agenda

  • @user-ic1zy4zj1c
    @user-ic1zy4zj1c หลายเดือนก่อน

    Mabwana a chawezi tamuchoseni uyu pa program imeneyi, we need balanced issues, awa ndi achibwana, a Mbuye Mulungu wa zonse mkatheni chawezi yu amen

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o หลายเดือนก่อน +1

    Kaliat ndi kathyali nfiti yaikaz

  • @GiftMathewe-fr3kn
    @GiftMathewe-fr3kn หลายเดือนก่อน

    Sanalakwise chifukwa zomwa adagwilrizana mungwilizano wawo palibe akuziwa

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza หลายเดือนก่อน

    Nkona anamuxhotsa ntchito ku mbc uyu xhitsiru wamva

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i หลายเดือนก่อน

    Palibe chifukwa cholembela kalata yothela ubalewawo nde asadijile kalata kodi mr chikangawawo atava zimezi anayitanapo a UTM kuti akambilane zakutuluka kwa UTM? Zomatiseka kumaso uwe chawezi uzingodya misokho ya amalawyo osatipusisa mene munkapanga zachipongwe ndichilima ndemumati atani palibeso zodikila myezi mafuna mugule UTM yose nde mwauponda mwakumananazo zanadulila muwona nyekgwe a MCP muwuzeni chimwendo abeleke over muzapenge gwilizano ndi ana achimwendo

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu หลายเดือนก่อน

    Ndipo monga ngati ine ndikuti anakhonza kwambili kutulukako mcp down

  • @Brihippo
    @Brihippo หลายเดือนก่อน

    Timafikila kuti chilima atiyakhule poti wamwalira a Patricia watiyakhula

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480 หลายเดือนก่อน

    Ayi choka iwe chawezi utm yachitabwino kutuluka musanga kt akozenyumba yawo even chilima akanavela kalindo bwezi izi kulibe lero winiko amanena zoona kt tulukani mu tose koma sanavele

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o หลายเดือนก่อน

    Utm yagulisa chipani ku dpp

  • @MaryMlongoti
    @MaryMlongoti หลายเดือนก่อน

    Chawezi umatha

  • @rabsonswathera738
    @rabsonswathera738 หลายเดือนก่อน

    Kuchoka mungwilizano kwachitika munthawi yake

  • @peterdanie4684
    @peterdanie4684 หลายเดือนก่อน

    Chawezi great analysis

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s หลายเดือนก่อน

    Ndipo achawezi sawlekeze kuonesa mutu ukakwela galimoto yako tikukhazula tionana aise manyi ako wanva

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c หลายเดือนก่อน +2

    Chisilu iweyo simadziwa Kuti Pali ndale kupha chilima

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v หลายเดือนก่อน

    Satana akalowa mpovuta kumutulusa, Chawezi amlowa satana.

  • @DamianoGabriel-sh2mf
    @DamianoGabriel-sh2mf หลายเดือนก่อน

    Chawezi capaign director wa mcp banja likatha palibe za ulemu

  • @jameshuwanzulu
    @jameshuwanzulu หลายเดือนก่อน

    Or ndi dzina lomwelo likungosonyeza kut ndi wa MCP

  • @estonmnthali3719
    @estonmnthali3719 หลายเดือนก่อน

    Chawezi ndi wa MCP

  • @idilissmuyer2914
    @idilissmuyer2914 หลายเดือนก่อน

    Pamtumbo panu inuyo mwasowa zokamba mamwapwala anu

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 หลายเดือนก่อน +1

    Ngati, mgwirizano unali wa anthu awiri basi uthepo winayo anatisiya ndiye UTM isiyeni

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y หลายเดือนก่อน +1

    Chawezi ndiwe Galu

  • @DysonUmali
    @DysonUmali หลายเดือนก่อน

    Whether the votes will be minus 20% we don't care . USI and the cabinet ministers can remain at MCP we don't care .The best Usi can do is to start his party and do the alliance with MCP . That will be his correct decision. He must not use UTM emblem because at UTM I don't see his impact achedwa kwambiri.

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c หลายเดือนก่อน +1

    Chawedzi ndiwe osokonedza

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 หลายเดือนก่อน +1

    Kod iweyo why ukukamira zimenezo ndiwe mbuzi et ?

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v หลายเดือนก่อน +1

    Iwe apanga nthawi yoyenera, afufuza bwanji za ifa ali ku tonse komweko? Aasa!

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl หลายเดือนก่อน

    Chawezi zinarakoro ndiramunthu wamukazi anakupasayo anakuwononga ndiye utisamare uzapezeka mumavuto mumene umamwera mowa iweyo🆗

  • @patrickmwakilasa7198
    @patrickmwakilasa7198 หลายเดือนก่อน

    Agalu inu

  • @samsonmtumbati4855
    @samsonmtumbati4855 หลายเดือนก่อน

    Programe iyi kulibwino angoyithetsa chifukwa zimene zimakambidwa akumapanga back up mcp so palibe Amalawi yingatithandize Programe yanuyi ayi just suspend it

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr หลายเดือนก่อน

    Kodi chawezi yu mumamutengelanji? Uyuyu adzandilakwitsa one day. Victor or abel, banda are the bes uyu ndiwa mcp. Sadzatheka Chawezi akupeza zabwino ku bomaku ndipo ativuta kulera 😅

  • @Chrissyluwe
    @Chrissyluwe หลายเดือนก่อน

    Chawez u hv no timing

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g หลายเดือนก่อน

    Chawezi samalira ayise we know ukulimbana ndi azipani zotsutsa samalira ayise I know you are there for mcp

  • @DysonUmali
    @DysonUmali หลายเดือนก่อน

    Chaweza what you should know is we didn't do a hasty decision . It a fine a decision and you can't change it.
    We are not desperate rather and we as voters cannot take it
    Chawezi you are MCP and no body can listen to your views .
    Member wa nzeru cannot proceed to be in alliance with MCP .

  • @petroszgambo9949
    @petroszgambo9949 หลายเดือนก่อน

    Useless program

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu หลายเดือนก่อน

    Achilima anali odekha mtima, koma ku bwela kwawo ulendo wakunja uja koria,anali ndicholinga chotuluka mu tonse kale, koma tsoka asanaphume kubwela kwaku koria ,ndimene amapita kumarilo akusambala posadziwa kuti awusi chisisi anakamuuza kale chakwela, kodi zonsetu tikuzidziwa koma ndalama ndalama, koma mulungu simuthu

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 หลายเดือนก่อน

    UTM IS NOT THE FIRST PARTY TO MOVE OUT OF THIS ALLIANCE , PEOPLE ARE TALKING ALOT BECAUSE IT HAS MANY YOUTH FOLLOWERS SO ZIKUBAYA ANTHU AMBIRI.

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i หลายเดือนก่อน +1

    Where is victor

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v หลายเดือนก่อน

    Chawezi uzafa ngati garu

  • @vincentkamangamr9062
    @vincentkamangamr9062 หลายเดือนก่อน

    Chawezi umawoneselatu kuti ndiwe wa MCP all times on this program

  • @DysonUmali
    @DysonUmali หลายเดือนก่อน

    In life ngati mkazi wakukana olo mutalankhula motani it's helpless to the man.
    UTM is done with MCP

  • @WilfredChinkono
    @WilfredChinkono หลายเดือนก่อน

    DK simunthu wamba UTM ikutenga boma 2025

  • @UsumanLuwayo
    @UsumanLuwayo หลายเดือนก่อน

    Ngati Dewesi ali pa banja njofunika kumunyengera mkadzi wake nde kupanga dzoti anthu adzamugwire mkadziyo akuchita chigololo nde iyeyo adzamve, then tidzaone ngati adzadekhe osathetsa banja antil 3 months

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx หลายเดือนก่อน

    Chawezi ndi wa chakwera

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb หลายเดือนก่อน

    Chawezi chawezi chawezi

  • @ChikuMatemba
    @ChikuMatemba หลายเดือนก่อน

    we don't like Chawezi on this Program

  • @BehindThecamera-xo1qg
    @BehindThecamera-xo1qg หลายเดือนก่อน

    Ulemu wa chani galu iwe chawezi, umamupasa ulemu munthu oipa

  • @BehindThecamera-xo1qg
    @BehindThecamera-xo1qg หลายเดือนก่อน

    Miyezi 4 inachuluka anthu ambiri akanasala ku mcp , achita bwino kutuluka fumbi la kuchikangawa lisanathe .

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl หลายเดือนก่อน

    Komatu chawedzi pena amayankhula ngati mbuli zedi kodi amene samadziwa kuti alliance ya utm ndi mcp inali yoti five yrs wina akhala president kenako wina azaimeso, ndi chifukwa ichi ndi chomwe chinabwelesa kusagwilizana cz ingakhale Dr late SKC ananena poyera kuti ngati Dr chakwera sakufuna kutula pansi udindo ndiye tiyenera tikavote. Utm kutuluka siinalakwise aii cz mcp siinalemekedze ingakhale imfa ya chilima mzinthu zambiri kumapanga msonkhano anthu akulilabe kenako uziti afulumira kutuluka ukhalike ndithu ngati akukunyemera tazingodya makobidiwo komano usaganize mombwambwana aiii

  • @user-lj7lm6ly7z
    @user-lj7lm6ly7z หลายเดือนก่อน

    Ine anthu awa amandionekera mwa mcp cp eeee ndiye aaaa sinkonda kunvera zamenewa

  • @user-cs6zy3ix8d
    @user-cs6zy3ix8d หลายเดือนก่อน

    Chawez ndi iwe mbuzi

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 หลายเดือนก่อน

    Chawezi wabodza iwe, sukuyenera kukhara analysis poti zuonekeratu ndiwe wa MCP

  • @PatrickDisple
    @PatrickDisple หลายเดือนก่อน

    He knows only how to speak but not to understand what he is speaking. Mr Chawezi 😅

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y หลายเดือนก่อน

    Ndi ntchito yawo,,,anali kuti? Nthawi yonseyi

  • @chimwemwechiundira6002
    @chimwemwechiundira6002 หลายเดือนก่อน

    Halayansi yabayatu

  • @tonnychimbiro
    @tonnychimbiro หลายเดือนก่อน

    Zinthu zake

  • @PiusChawinga
    @PiusChawinga หลายเดือนก่อน

    Wabweza bwanji?

  • @user-my5jj5we5j
    @user-my5jj5we5j หลายเดือนก่อน

    Unuso mukuziwa mugwilizano panalibe

  • @KestonNGUBO
    @KestonNGUBO หลายเดือนก่อน

    Zoonad iwe

  • @user-gy8yn6qw2k
    @user-gy8yn6qw2k หลายเดือนก่อน

    Ineyo i don't like this guy is not the best for me ........

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 หลายเดือนก่อน

    Chawezi ma comments ako ngooneseratu uli mbali yinayo uli against UTM