- 16
- 368 528
MALAWI TODAY
South Africa
เข้าร่วมเมื่อ 18 ก.ย. 2022
This Channel aims to inform, educate, Entertain and help Malawians.
วีดีโอ
ZOMWE WANKHULA MICHAEL USI KU KHWIMBI LA OTSATIRA UTM KU MZUZU
มุมมอง 3219 ชั่วโมงที่ผ่านมา
ZOMWE WANKHULA MICHAEL USI KU KHWIMBI LA OTSATIRA UTM KU MZUZU
NORMAN CHISALE Wachenjeza komanso kupeleka chiophyezo kwa anyamata a MCP
มุมมอง 2.8K9 ชั่วโมงที่ผ่านมา
NORMAN CHISALE Wachenjeza komanso kupeleka chiophyezo kwa anyamata a MCP
Prophet Habakukk Chikondi Chakhodzokera😁
มุมมอง 106วันที่ผ่านมา
Prophet Habakukk Chikondi Chakhodzokera😁
ACHAKWERA SANAGONE KUCHIPANI KOMA AKUGONA KU BOMA
มุมมอง 149วันที่ผ่านมา
ACHAKWERA SANAGONE KUCHIPANI KOMA AKUGONA KU BOMA
KULANKHULA KWA JOICE BANDA (11 Aug 2024)
มุมมอง 122วันที่ผ่านมา
KULANKHULA KWA JOICE BANDA (11 Aug 2024)
VITUMBIKO MUMBA KUYAMBAPO KUTIMBWATIKA
มุมมอง 879หลายเดือนก่อน
VITUMBIKO MUMBA KUYAMBAPO KUTIMBWATIKA
JOSHUA VARELA KUDZUDZULA MKHALIDWE OIPA OKHUDZA IMFA YA SAULOS CHILIMA
มุมมอง 83Kหลายเดือนก่อน
JOSHUA VARELA KUDZUDZULA MKHALIDWE OIPA OKHUDZA IMFA YA SAULOS CHILIMA
MDIPITI WODABWITSA WA MAGALIMOTO😳 PRESIDENT LAZARUS CHAKWERA
มุมมอง 7Kหลายเดือนก่อน
Intensified security convoy of the president of Malawi
Zoona A President Tizikhalira Kukukuwani? Wonder Akutero. 8 Oct 2023
มุมมอง 12K10 หลายเดือนก่อน
Zoona A President Tizikhalira Kukukuwani? Wonder Akutero. 8 Oct 2023
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke// PART 2
มุมมอง 50K10 หลายเดือนก่อน
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke// PART 2
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
มุมมอง 192K10 หลายเดือนก่อน
JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1
Big up Mr kapito And God bless you
Malawi its 4 malawians not 4 mr chikangawa tru speaking mr kapito A.P.M our vote
Thats true sakudziwa za boma ,palibe akudziwa za u presdent thts why wangosanduka chigawenga
God bless you mwamasuka kuuza a malawi
That's number one Mr kapito speaking as a man of integrity
My vote
Zoona,zoona A.P.M wawina kale olo mr chikangawa olo adzabele sizizanukha kanthu adzipita gwape amenei D.P.P oyee!
Woyeeeeee❤❤
Ife tikufuna tidzidya msima kuyambila mamawa,masana,madzulo, usiku imeneo nde D.P.P
🔥🔥🔥
Bodza ili, mavuto adalipo kuchokera nthawi ya kamuzu, Komaso inuwo a Dpp. Nthawi imene mudali boma bwanji wosathetsa mavutowo.
Professor afa peter muthalika😂
😂😂😂😂
Mcp ndimbola achuluka ndi anthu ufuna kusilemereza okha osanganizira mavuto awena
kugulidwa kotai koditu zamavuto alipano sikuti munthu ungsmunsmize
Mr Chisale more fire❤❤❤❤❤❤ Ndasangalala kwambiri kut mwawina❤❤❤ Tikufuna chitetezo cha mphamvu zeeeeeedi kwa Adad❤
Ife timuvoteraso Chakwera! Dowa yake iti inu munamepo apa! Anthu atatu oti angogulidwa ndiye kumati Dowa ingavotele nkhalamba yosankha mitunduyo
Achewa inu ndi agalu chifukwa mavuto alipanopa sakuwona kuti uyu anavotela mcp tonse tikulila limozi
Tsankho silingapose zomwe aluchita Chakwera ni nyau zinzake. Tsano anthu ali ni ufulu osankhula uyo alufuna. Dziko sila Chakwera ili ayi.
iwe ndichisiru osaganiza ndi chikangawa wakoy akupas zingat kut uzilakhula zoduka mutu galu ukuvutikaso chitsiru iwe ubwin wake tonse tikugula zodula limoz
Inuso inu nde opanda nzerudi Kutengela kuti ndi ochewa onzanu Muluvutika or panado muzipatala Tsankho lipose asùweni akowo opatsa udindo okhaokha khalabe usasunthe uwone 2025 Poti mudzabela mpake mukukula matako
Iweso uli wekha don't be stupid
Muto ndi la kupha chilima
DPP Moto Kuti buuuu
Amalawi ozindikila kwambiri
Si Dowa ya genuine iyi. DPP siingaphule kanthu ku Dowa. Ochita kugulidwa awa kuti abebetse DPP. Phuma chipani cha DPP, kuwina sikulongolola-owina 2025 ali phee. You can tell kuti anthu awa nga phuma through their leader's speech. A Mutharika kuyankhula mbwelera yokhayokha ngati kuti ma voters onse ali mmanja mwawo."Dikira madzi apite ndipo uziti ndadala".
Mot lwe sukuwona mavutowo lne kwanthu ndikasungu Koma sininganene Za chikangawa Kut wapanga chitukuko
@@FrancisMazamba Waboza iwe ukungopanga disguise. Chakwera ndi dolo osati zinazi.
@@tasmania527 udolo wake pakupha chilima ndi ena aja ndi uchigawenga mzomwe akukwanisa plus kugwesa kwacha daily, mkuthwa mkamwa kma pa ground ndi 0/10
Ndi brother wanga uyu from dowa Ndithu Sanagulidwensoi unama zed mmmmm
@MzadziWanga Don't forget kuti munatiphela anthu 20 ku mzuzu, munapha ma Albino, munapha Njaunju, munapha Chasowa. Imfa ya Chilima yinali ngozi chifukwa ndege yinali yakutha ndipo mulibe umboni woti anaphedwa, nde shut up.Nkhanza zanu ndi kuyipa kwanu mumachita kunyada nako ndipo zinali pa mbalambanda.
Anzawo akugaula nursery pano... Anthu awulesi awa
koma zomwe akuyakhulaz ukuzimveses bwino lomwe chikangawa iwe
Ulesi ndiwe osati Zagwilizana pati Mudamuphelanji chilima asatana inu
achewatu amenewo chilungamo kuyenda ngati manzi
Chilungamotu chimenechi osaopatu osafooka osatopa kkkk
Awa tikakumana Ku conversion
koma chisale amandipats mantha kut uyuyu kupeze kut wawina koma mwati dzikoli izayenda bwanji
Uremuwani mama
Mumakwana akweni
Ndipo a Kweni ayankha mwa ulemu a aka khala Brian banda eeee tinakaonatu zinthu nda kweni
Kweni woyeee
A Kaliati poti apa akukuitanirani ku DPP kumeneko mukakhala nobody zonse mukukamba apazi zizatheka muzidzangolira kuti wa PA CARRIER SAIMBA BELU
Akweni munangokhala mzimai koma ndinu katundu
nkweni umakwana
Zoona mama,,yankhulani
Good speach welcome aKweni❤
Good speach welcome aKweni❤
Mumakhwana kwene
Munthu oyipa anagulitsa chipani
Achunga why has he failed Malawi, time has told. He owns the good and the bad.
Zosangalasa kwambiri kuti woluza akuvomeleza ndikulonjeza kupita chisogolo kugwira ntchito ndi omwe apambana,izi zasonyeza kuti MCP Ndichipani cha mtendere komanso chokondana wina ndi mzake ngati banja limodzi.MCP 2025 ndiyo wina kale,yayika foundation ya bwino kwambiri kuyambila pa convention kukasilizila kuma region ndima district.what a beautiful picture displayed by MCP Party.This sends a clear signal of strategic and mature leadership of president Dr Lazarus maccarthy chakwera.❤❤❤❤❤❤❤
Kapito , you say infact so God bless you plus
Zoonadi nkhaniyo ndiyowona
Kapito is a genius
😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Mr.Kapito your now talking. Kodi Aboma Samamvela mfundo ngati zimenezi bwanji kuti Dziko lathu nkutukukako.Ambuye akudalitseni nonse ogwiritsa ntchito mau amenewa
Very clear
Hi
Mtima udakawawabe ine 😢😢😢😢
Yes indeed
😂😂😂😂😂 palibe, mkapune
Mbava ngati iwe angakuvotere ndani waba iba ndi nick cakwera lero ufuna upitilidze kuba
Komano akubanja mwaiwala kutiko chilima anali ndani ... anthutu sasiya kupitako kumandako coz muthu uja anthu amamukonda